Unknown - Malaysia Native Anthem Text Lyrics






# A B C D E F G H I J K L M N O P Q R S T U V W X Y Z
Soundtracks






Unknown Lyrics

Malaysia Native Anthem Text Lyrics


1.
Mlungu dalitsani Malawi,
Mumsunge m'mtendere.
Gonjetsani adani onse,
Njala, nthenda, nsanje.
Lunzitsani mitima yathu,
Kuti tisaope.
Mdalitse Mtsogo leri na fe,
Ndi Mai Malawi.
2.
Malawi ndziko lokongola,
La chonde ndi ufulu,
Nyanja ndi mphepo ya m'mapiri,
Ndithudi tadala.
Zigwa, mapiri, nthaka, dzinthu,
N'mphatso zaulere.
Nkhalango, madambo abwino.
Ngwokoma Malawi.
3.
O! Ufulu tigwirizane,
Kukweza Malawi.
Ndi chikondi, khama, kumvera,
Timutumikire.
Pa nkhondo nkana pa mtendere,
Cholinga n'chimodzi.
Mai, bambo, tidzipereke,
Pokweza Malawi.
Sent by Carlos André Pereira da Silva Branco




Soundtracks
A B C D E F G H I J K L M N O P Q R S T U V W X Y Z #



 

Notice: All lyrics are the sole property of the indicated authors. Many lyrics have been transcribed by ear and may contain inaccuracies.